Bungwe la World Bank lalonjeza kuthandiza dziko la Malawi ndi ndalama zokwana $350Million kuti zithandize ntchito yomanga malo opukusira magetsi a Mpatamanga Hydropower Project. Bank yaikuluyi yalengeza izi kupereka mudziko la America pamsonkhano wadzachuma wa World economic Summit (WES). Izi zatheka kamba ka utsogoleri wabwino wa Dr Lazarus McCarthy Chakwera omwe akuimilidwa ndi nduna ya zachuma a Simplex Chithyola Banda. Malo amenewa azipanga mphamvu za magetsi zokwama 361Megawatts. Akatswiri ayamikira izi kuti zithandiza kutukula chuma cha dziko lino. Post navigation K9 million up for grabs as NBM Plc wraps upĀ ‘Popanda Chifukwa’Ā Promotion Katoto Supermarket hikes Mzuzu netball sponsorship to K5 million